Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 8:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Kenako ndinalamula kuti tisale kudya tili kumtsinje wa Ahava kuja, kuti tidzichepetse+ pamaso pa Mulungu wathu ndi kumupempha kuti atisonyeze njira yoyenera+ kwa ife, ana athu,+ ndi katundu wathu yense.

  • Salimo 78:52
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 52 Kenako anachititsa anthu ake kuchoka m’dzikolo ngati gulu la nkhosa,+

      Anawayendetsa m’chipululu ngati gulu la ziweto.+

  • Yesaya 30:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Makutu ako adzamva mawu kumbuyo kwako, akuti: “Njira ndi iyi.+ Yendani mmenemu anthu inu.” Yendani m’njira imeneyi kuti musasochere n’kulowera kudzanja lamanja kapena lamanzere.+

  • 2 Petulo 2:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Zikanakhala bwino akanapanda kudziwa molondola njira ya chilungamo,+ kusiyana n’kuidziwa bwinobwino kenako n’kupatuka pa lamulo loyera lomwe anapatsidwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena