Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 33:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Iye wandiwombola kuti ndisapite kudzenje,+

      Ndipo moyo wanga udzaona kuwala.’

  • Salimo 30:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, mwanditulutsa m’Manda,+

      Mwandisunga ndi moyo, kuti ndisatsikire m’dzenje.+

  • Salimo 49:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma Mulungu adzawombola moyo wanga ku Manda,+

      Pakuti adzandilandira. [Seʹlah.]

  • Salimo 56:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pakuti inu mwalanditsa moyo wanga ku imfa.+

      Inu mwateteza phazi langa kuti lisapunthwe,+

      Kuti ndiyendeyende pamaso pa Mulungu m’kuwala kumene kumaunikira anthu amoyo.+

  • Salimo 103:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Tamanda amene akuwombola moyo wako kudzenje,+

      Amene akukuveka kukoma mtima kosatha ndi chifundo ngati chisoti chachifumu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena