Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mitunduyo udzaiswa ndi ndodo yachifumu yachitsulo,+

      Udzaiphwanya ngati mbiya yadothi, n’kukhala zidutswazidutswa.”+

  • Salimo 45:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndipo upambane mu ulemerero wako.+

      Kwera pahatchi yako chifukwa cha choonadi, kudzichepetsa ndi chilungamo,+

      Ndipo dzanja lako lamanja lidzakulangiza mu zinthu zochititsa mantha.+

  • Salimo 45:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mivi yako yakuthwa idzalasa mitima ya adani a mfumu,+

      Mitundu ya anthu idzagwa pamapazi ako.+

  • Mateyu 24:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Pamenepo chizindikiro cha Mwana wa munthu+ chidzaonekera kumwamba. Ndiyeno mafuko onse a padziko lapansi adzadziguguda pachifuwa chifukwa cha chisoni,+ ndipo adzaona Mwana wa munthu akubwera pamitambo ya kumwamba ndi mphamvu ndi ulemerero waukulu.+

  • Luka 19:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Komanso adani angawa, amene sanafune kuti ine ndikhale mfumu yawo, bwerani nawo kuno muwaphe ine ndikuona.’”+

  • Chivumbulutso 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Taonani! Akubwera ndi mitambo,+ ndipo diso lililonse lidzamuona,+ ngakhalenso anthu amene anamulasa.+ Ndipo mafuko onse a padziko lapansi adzadziguguda pachifuwa ndi chisoni chifukwa cha iye.+ Ame.

  • Chivumbulutso 6:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Nditayang’ana, ndinaona hatchi* yoyera.+ Wokwerapo+ wake ananyamula uta.+ Iye anapatsidwa chisoti chachifumu,+ ndi kupita kukagonjetsa adani ake+ ndipo anapambana pa nkhondo yolimbana nawo.+

  • Chivumbulutso 11:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Koma mitundu ya anthu inakwiya, ndipo mkwiyo wanu unafika. Inafikanso nthawi yoikidwiratu yakuti akufa aweruzidwe, nthawi yopereka mphoto+ kwa akapolo anu aneneri,+ ndiponso kwa oyerawo, ndi oopa dzina lanu, olemekezeka ndi onyozeka omwe.+ Komanso, nthawi yowononga+ amene akuwononga dziko lapansi.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena