Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 19:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Malamulo+ ochokera kwa Yehova ndi olungama,+ amasangalatsa mtima.+

      Chilamulo+ cha Yehova ndi choyera,+ chimatsegula maso.+

  • Salimo 33:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Pakuti mawu a Yehova ndi owongoka,+

      Ndipo ntchito zake zonse ndi zodalirika.+

  • Salimo 119:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Inu mwatilamula kuti tisunge+

      Malamulo anu mosamala.+

  • Yesaya 55:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 ndi mmenenso adzakhalire mawu otuluka pakamwa panga.+ Sadzabwerera kwa ine popanda kukwaniritsa cholinga chake,+ koma adzachitadi zimene ine ndikufuna+ ndipo adzakwaniritsadi zimene ndinawatumizira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena