Salimo 19:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Malamulo+ ochokera kwa Yehova ndi olungama,+ amasangalatsa mtima.+Chilamulo+ cha Yehova ndi choyera,+ chimatsegula maso.+ Salimo 111:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Ntchito za manja ake zimadziwika ndi choonadi ndiponso chiweruzo.+נ [Nun]Malamulo onse amene amapereka ndi odalirika.+ Salimo 119:93 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 93 Sindidzaiwala malamulo anu mpaka kalekale,+Chifukwa mwandisungabe wamoyo kudzera m’malamulo amenewo.+ Salimo 119:100 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 100 Ndimachita zinthu mozindikira kuposa anthu achikulire,+Chifukwa ndimasunga malamulo anu.+ Salimo 119:173 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 173 Dzanja lanu lindithandize,+Chifukwa ndasankha malamulo anu.+
8 Malamulo+ ochokera kwa Yehova ndi olungama,+ amasangalatsa mtima.+Chilamulo+ cha Yehova ndi choyera,+ chimatsegula maso.+
7 Ntchito za manja ake zimadziwika ndi choonadi ndiponso chiweruzo.+נ [Nun]Malamulo onse amene amapereka ndi odalirika.+ Salimo 119:93 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 93 Sindidzaiwala malamulo anu mpaka kalekale,+Chifukwa mwandisungabe wamoyo kudzera m’malamulo amenewo.+ Salimo 119:100 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 100 Ndimachita zinthu mozindikira kuposa anthu achikulire,+Chifukwa ndimasunga malamulo anu.+ Salimo 119:173 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 173 Dzanja lanu lindithandize,+Chifukwa ndasankha malamulo anu.+
93 Sindidzaiwala malamulo anu mpaka kalekale,+Chifukwa mwandisungabe wamoyo kudzera m’malamulo amenewo.+