Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 6:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Yehova akuyang’aneni mokondwera+ ndipo akupatseni mtendere.”’+

  • Salimo 80:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Inu Mulungu wa makamu, tibwezeretseni mwakale.+

      Walitsani nkhope yanu kuti tipulumutsidwe.+

  • Salimo 89:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Odala ndi anthu amene amafuula mosangalala.+

      Iwo amayendabe m’kuwala kwa nkhope yanu, inu Yehova.+

  • Salimo 119:135
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 135 Ndikomereni mtima ine mtumiki wanu,+

      Ndipo ndiphunzitseni malamulo anu.+

  • Miyambo 16:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Nkhope ya mfumu ikawala, zimatanthauza moyo.+ Ndipo mafuno ake abwino ali ngati mtambo wa mvula yomalizira.+

  • 1 Petulo 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pakuti maso+ a Yehova* ali pa olungama, ndipo makutu ake amamva pembedzero lawo,+ koma nkhope ya Yehova imakwiyira anthu ochita zoipa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena