Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 25:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 “‘M’bale wanu akasauka pakati panu+ ndipo sangathe kudzisamala, muzim’thandiza.+ Iye ayenera kukhala ndi moyo mmene mlendo wokhala pakati panu+ alili ndi moyo.

  • Deuteronomo 15:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Wina mwa abale ako akasauka pakati panu, mu umodzi mwa mizinda yanu, m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa, usamuumire mtima kapena kumuumitsira dzanja lako.+

  • Salimo 37:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Tsiku lililonse amakomera mtima ena ndi kuwakongoza zinthu,+

      Ndipo ana ake adzalandira madalitso.+

  • Salimo 112:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Munthu wachisomo+ komanso wokongoza ena zinthu ndi wabwino.+

      י [Yohdh]

      Amachita zinthu mwachilungamo.+

  • 2 Timoteyo 1:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ambuye achitire chifundo banja la Onesiforo,+ chifukwa iye anali kubwera kawirikawiri kudzandilimbikitsa,+ ndipo sanachite manyazi ndi maunyolo anga.+

  • Aheberi 13:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Komanso, musaiwale kuchita zabwino+ ndi kugawana zinthu ndi ena, pakuti nsembe zotero Mulungu amakondwera nazo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena