Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 58:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Oipa akhala opotoka maganizo kuyambira ali m’mimba.+

      Iwo asochera kuyambira ali m’mimba,

      Ndipo amalankhula zabodza.+

  • Miyambo 22:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Uchitsiru umakhazikika mumtima mwa mwana.+ Koma ndodo yomulangira* ndi imene imauthamangitsira kutali ndi iye.+

  • Mateyu 7:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Momwemonso mtengo uliwonse wabwino umabala zipatso zabwino, koma mtengo uliwonse wovunda umabala zipatso zopanda pake.+

  • Luka 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 chifukwa adzakhala wamkulu pamaso pa Yehova.+ Koma asadzamwe vinyo ngakhale pang’ono+ kapena chakumwa chaukali chilichonse. Ndipo adzadzazidwa ndi mzimu woyera kuyambira ali m’mimba mwa mayi ake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena