Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 15:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Nadabu+ mwana wa Yerobowamu anakhala mfumu ya Isiraeli m’chaka chachiwiri cha Asa mfumu ya Yuda, ndipo anapitiriza kulamulira Isiraeli kwa zaka ziwiri.

  • 1 Mafumu 16:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 M’chaka cha 26 cha Asa mfumu ya Yuda, Ela mwana wa Basa anakhala mfumu ya Isiraeli ku Tiriza kwa zaka ziwiri.

  • 1 Mafumu 16:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 M’chaka cha 27 cha Asa mfumu ya Yuda, Zimiri anakhala mfumu ku Tiriza kwa masiku 7.+ Pa nthawiyo anthu anali atamanga msasa pafupi ndi mzinda wa Gebetoni,+ umene unali wa Afilisiti, kuti authire nkhondo.

  • 1 Mafumu 16:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Pomalizira pake, anthu amene anali kutsatira Omuri anagonjetsa otsatira Tibini mwana wa Ginati. Choncho Tibini anafa, ndipo Omuri anayamba kulamulira.

  • 2 Mbiri 36:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Yehoahazi anali ndi zaka 23 pamene anayamba kulamulira, ndipo analamulira miyezi itatu ku Yerusalemu.+

  • Hoseya 13:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiyeno ndinakupatsa mfumu nditakwiya+ ndipo ndidzaichotsa nditakwiya.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena