Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Yembekezera Yehova, ndi kusunga njira zake,+

      Ndipo adzakukweza kuti ulandire dziko lapansi.+

      Pamene oipa akuphedwa, iwe udzaona.+

  • Salimo 58:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Wolungama adzasangalala chifukwa chakuti waona oipa akupatsidwa chilango.+

      Adzasambitsa mapazi ake m’magazi a anthu oipa.+

  • Salimo 91:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Udzayang’ana ndi maso ako,+

      Ndipo udzaona anthu oipa akulandira chilango.+

  • Chivumbulutso 18:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “Kondwerani kumwambako+ chifukwa cha zimene zamuchitikira. Inunso oyera,+ inu atumwi,+ ndi inu aneneri, kondwerani chifukwa Mulungu wamuweruza ndi kumupatsa chilango chifukwa cha zomwe anakuchitirani.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena