Esitere 6:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Hamani atalowa, mfumu inam’funsa kuti: “Kodi munthu amene mfumu yafuna kum’patsa ulemu tim’chitire chiyani?”+ Atamva zimenezi, Hamani ananena mumtima mwake kuti: “Kodi winanso ndani amene mfumu ingafune kum’patsa ulemu kuposa ine?”+ Miyambo 18:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Munthu asanagwe, mtima wake umadzikweza,+ ndipo asanapeze ulemerero, amadzichepetsa.+ Luka 18:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Ndithu ndikukuuzani, Munthu ameneyu anapita kwawo ataonedwa kukhala wolungama kwambiri+ kusiyana ndi wina uja, chifukwa aliyense wodzikweza adzam’nyazitsa, koma wodzichepetsa adzamukweza.”+ Yakobo 4:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Komabe, kukoma mtima kwakukulu kumene Mulungu amapereka kumaposa khalidwe limeneli.+ N’chifukwa chake lemba limati: “Mulungu amatsutsa odzikweza,+ koma odzichepetsa amawasonyeza kukoma mtima kwake kwakukulu.”+
6 Hamani atalowa, mfumu inam’funsa kuti: “Kodi munthu amene mfumu yafuna kum’patsa ulemu tim’chitire chiyani?”+ Atamva zimenezi, Hamani ananena mumtima mwake kuti: “Kodi winanso ndani amene mfumu ingafune kum’patsa ulemu kuposa ine?”+
14 Ndithu ndikukuuzani, Munthu ameneyu anapita kwawo ataonedwa kukhala wolungama kwambiri+ kusiyana ndi wina uja, chifukwa aliyense wodzikweza adzam’nyazitsa, koma wodzichepetsa adzamukweza.”+
6 Komabe, kukoma mtima kwakukulu kumene Mulungu amapereka kumaposa khalidwe limeneli.+ N’chifukwa chake lemba limati: “Mulungu amatsutsa odzikweza,+ koma odzichepetsa amawasonyeza kukoma mtima kwake kwakukulu.”+