Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Rute 3:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Tsopano usachite mantha mwana wanga. Ndidzakuchitira zonse zimene wanena,+ chifukwa aliyense mumzinda wathu akudziwa kuti ndiwe mkazi wabwino kwambiri.+

  • Miyambo 12:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Mkazi wabwino ndi chisoti cha ulemu kwa mwamuna wake,*+ koma mkazi wochita zinthu zochititsa manyazi ali ngati chowoletsa mafupa a mwamunayo.+

  • Miyambo 19:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Cholowa chochokera kwa makolo ndicho nyumba ndi chuma,+ koma mkazi wanzeru amachokera kwa Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena