Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 24:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Rabekayo anayankha kuti: “Eni, imwani mbuyanga.” Atatero anatsitsa mtsuko wake mwamsanga n’kuupendeketsa kuti mtumikiyo amwe.+

  • Yoswa 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 (Koma iye anali atawatengera padenga,*+ ndi kuwabisa pansi pa mapesi a fulakesi* padengapo.)

  • 2 Mafumu 4:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tiyeni tim’mangire kachipinda kapadenga*+ kukhoma.* M’kachipindamo timuikire bedi, tebulo, mpando, ndi choikapo nyale,+ kuti akabwera azikhala mmenemo.”+

  • Machitidwe 16:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Tsopano iye ndi a m’banja lake atabatizidwa,+ anachonderera kuti: “Abale ngati inu mwaona kuti ndine wokhulupirika kwa Yehova, tiyeni mukalowe m’nyumba yanga ndi kukhala mmenemo.”+ Moti anatiumiriza ndithu kupita kwawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena