Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 9:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Kenako Yehu anafika ku Yezereeli,+ ndipo Yezebeli+ anamva zimenezo. Yezebeliyo anadzikongoletsa podzipaka utoto+ wakuda m’maso mwake n’kukongoletsanso tsitsi lake mochititsa kaso.+ Atatero anakaima pawindo n’kumayang’ana kunja.+

  • Esitere 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 kuti abweretse Mfumukazi Vasiti itavala duku lachifumu pamaso pa mfumu, kuti anthu onse ndi akalonga aone kuoneka bwino kwake, pakuti inalidi yokongola kwambiri.+

  • Miyambo 6:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Usasirire kukongola kwake mumtima mwako.+ Asakukope ndi maso ake owala,+

  • 1 Petulo 1:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Pakuti “anthu onse ali ngati udzu, ndipo ulemerero wawo wonse uli ngati duwa la udzu.+ Udzuwo umafota ndipo duwalo limathothoka,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena