Ekisodo 33:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Ndiyeno Yehova analankhulanso ndi Mose kuti: “Uza ana a Isiraeli kuti, ‘Inu ndinu anthu ouma khosi.+ Ndingathe kulowa pakati panu ndi kukufafanizani m’kamphindi.+ Chotero, vulani zodzikongoletsera, pakuti ndikufuna kuona choti ndikuchiteni.’”+ 2 Mbiri 29:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Pakuti makolo athu achita zosakhulupirika+ ndipo achita zoipa pamaso pa Yehova Mulungu wathu.+ Iwo anamusiya+ n’kufulatira chihema chopatulika cha Yehova+ n’kulozetsako nkhongo. Yeremiya 5:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 “Iwo akana Yehova, ndipo akunena kuti, ‘Iye kulibe.+ Ndipo ife tsoka silidzatigwera. Sitidzaona lupanga lililonse kapena njala yaikulu.’+
5 Ndiyeno Yehova analankhulanso ndi Mose kuti: “Uza ana a Isiraeli kuti, ‘Inu ndinu anthu ouma khosi.+ Ndingathe kulowa pakati panu ndi kukufafanizani m’kamphindi.+ Chotero, vulani zodzikongoletsera, pakuti ndikufuna kuona choti ndikuchiteni.’”+
6 Pakuti makolo athu achita zosakhulupirika+ ndipo achita zoipa pamaso pa Yehova Mulungu wathu.+ Iwo anamusiya+ n’kufulatira chihema chopatulika cha Yehova+ n’kulozetsako nkhongo.
12 “Iwo akana Yehova, ndipo akunena kuti, ‘Iye kulibe.+ Ndipo ife tsoka silidzatigwera. Sitidzaona lupanga lililonse kapena njala yaikulu.’+