Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 14:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ana ake amalemekezedwa, koma iye sadziwa zimenezo.+

      Iwo amakhala opanda pake, koma iye sawaganizira.

  • Miyambo 27:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Usadzitame ndi zamawa+ chifukwa sukudziwa zimene zidzachitike mawa.+

  • Mlaliki 8:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pakuti palibe akudziwa zimene zidzachitike,+ popeza ndani angamuuze mmene zidzachitikire?

  • Yakobo 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mumatero chonsecho simukudziwa kuti moyo wanu udzakhala wotani mawa.+ Pakuti ndinu nkhungu yongoonekera kanthawi kenako n’kuzimiririka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena