Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mlaliki 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pakuti ana a anthu ali ndi mapeto, ndipo zinyamanso zili ndi mapeto. Mapeto a zonsezi ndi ofanana.+ Nyama imafa ndipo munthunso amafa.+ Mzimu wa zonsezi ndi umodzi,+ moti munthu saposa nyama, pakuti zonse n’zachabechabe.

  • Mlaliki 9:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Zimene zimachitikira anthu onse n’zofanana.+ Pali mapeto amodzi+ kwa munthu wolungama+ ndi woipa,+ kwa munthu wabwino, woyera, ndi wodetsedwa, ndiponso kwa munthu amene amapereka nsembe ndi amene sapereka nsembe. Munthu wabwino n’chimodzimodzi ndi munthu wochimwa.+ Munthu amene amalumbira mosaganizira bwino n’chimodzimodzi ndi amene amaopa kulumbira.+

  • Mlaliki 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Nditaganizanso ndinaona kuti padziko lapansi pano anthu othamanga kwambiri sapambana pampikisano,+ amphamvu sapambana pankhondo,+ anzeru sapeza chakudya,+ omvetsa zinthu nawonso sapeza chuma,+ ndipo ngakhale odziwa zinthu sakondedwa,+ chifukwa nthawi yatsoka ndi zinthu zosayembekezereka zimagwera onsewo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena