Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 23:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ulamuliro wake umakhala ngati kuwala kwa m’mawa pamene dzuwa lawala,+

      M’mawa wopanda mitambo.

      Umakhala ngati msipu womera padziko mvula ikakata, dzuwa n’kuwala.’+

  • Yesaya 58:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Mukatero kuwala kwanu kudzaonekera ngati m’bandakucha,+ ndipo mudzachira mofulumira kwambiri.+ Chilungamo chanu chizidzayenda patsogolo panu,+ ndipo ulemerero wa Yehova uzidzalondera kumbuyo kwanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena