Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 16:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndipo uzisangalala pa chikondwerero chimenecho,+ iweyo, mwana wako wamwamuna, mwana wako wamkazi, kapolo wako wamwamuna, kapolo wako wamkazi, Mlevi, mlendo wokhala pakati panu, mwana wamasiye ndi mkazi wamasiye, amene ali mumzinda wanu.

  • Salimo 42:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndidzakumbukira zinthu zakale ndipo moyo wanga udzavutika pokumbukira zimenezo.+

      Pakuti ndinali kuyenda ndi khwimbi la anthu,

      Ndinali kuyenda pang’onopang’ono patsogolo pawo kupita kunyumba ya Mulungu,+

      Tinali kufuula mosangalala ndi kuyamika Mulungu.+

      Khamu la anthu okondwerera madyerero linali kunditsatira.+

  • Salimo 81:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yambani kuimba nyimbo+ ndipo tengani maseche,+

      Zeze womveka mosangalatsa pamodzi ndi choimbira cha zingwe.+

  • Mateyu 26:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Potsirizira pake, atatha kuimba nyimbo zotamanda Mulungu,+ anatuluka n’kupita kuphiri la Maolivi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena