Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Adzaopa ndipo adzagwidwa ndi mantha aakulu.+

      Chifukwa cha dzanja lanu lamphamvu, adzakhala chete ngati mwala.

      Kufikira anthu anu+ atadutsa, inu Yehova,

      Kufikira anthu anu amene munawapanga+ atadutsa.+

  • Salimo 98:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 98 IMBIRANI Yehova nyimbo yatsopano,+

      Pakuti zimene wachita ndi zodabwitsa.+

      Dzanja lake lamanja, ndithu mkono wake woyera, wabweretsa chipulumutso.+

  • Yesaya 53:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 53 Kodi ndani wakhulupirira zimene ife tamva?+ Ndipo kodi dzanja la Yehova+ laonetsedwa kwa ndani?+

  • Luka 1:51
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 51 Wachita zamphamvu ndi dzanja lake,+ wabalalitsira kutali odzikweza m’zolinga za mitima yawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena