Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 72:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mapiri atenge mtendere ndi kupita nawo kwa anthu,+

      Komanso zitunda zitenge mtendere wopezeka mwachilungamo.

  • Salimo 119:165
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 165 Okonda chilamulo chanu amapeza mtendere wochuluka,+

      Ndipo palibe chowakhumudwitsa.+

  • Yesaya 55:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Pakuti anthu inu mudzachoka ndi chisangalalo+ ndipo mudzafika ndi mtendere.+ Mapiri ndi zitunda zidzakusangalalirani ndi mfuu yachisangalalo,+ ndipo mitengo yonse yakutchire idzawomba m’manja.+

  • Aroma 14:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pakuti ufumu wa Mulungu+ si kudya ndi kumwa ayi,+ koma chilungamo,+ mtendere+ ndi chimwemwe+ zobwera ndi mzimu woyera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena