Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 18:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 M’chaka cha 14 cha Mfumu Hezekiya, Senakeribu+ mfumu ya Asuri+ anabwera kudzachita nkhondo ndi mizinda yonse ya Ayuda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri, ndipo analanda mizindayo.

  • 2 Mbiri 28:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ahazi anatenga zinthu za m’nyumba ya Yehova,+ za m’nyumba ya mfumu+ ndi za m’nyumba za akalonga,+ n’kuzipereka kwa mfumu ya Asuri+ monga mphatso, koma zimenezi sizinam’thandize.

  • Yesaya 10:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Eya! Msuri+ ndiye ndodo ya mkwiyo wanga+ komanso chikwapu chosonyezera ukali wanga chimene chili m’dzanja lake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena