-
Salimo 17:13Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
13 Nyamukani, inu Yehova, yang’anizanani naye maso ndi maso woipayo.+
M’gonjetseni. Pulumutsani moyo wanga kwa woipayo ndi lupanga lanu.+
-
Yeremiya 46:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 “Limeneli ndi tsiku la Yehova wa makamu, Ambuye Wamkulu Koposa ndipo ndi tsiku lobwezera chilango kwa adani ake.+ Lupanga lidzadya adaniwo ndi kukhuta ndipo lidzamwa magazi awo kufikira litathetsa ludzu lake. Lidzatero pakuti Yehova wa makamu, Ambuye Wamkulu Koposa,+ ali ndi nsembe imene akufuna kupereka+ m’dziko la kumpoto, m’mphepete mwa mtsinje wa Firate.+
-
-
-