Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ndikanoladi lupanga langa lonyezimira,+

      Dzanja langa likagwira chiweruzo,+

      Ndidzalipsira adani anga,+

      Ndipo ndidzabwezera chilango kwa odana nane kwambiri.+

  • Salimo 17:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Nyamukani, inu Yehova, yang’anizanani naye maso ndi maso woipayo.+

      M’gonjetseni. Pulumutsani moyo wanga kwa woipayo ndi lupanga lanu.+

  • Yeremiya 46:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Limeneli ndi tsiku la Yehova wa makamu, Ambuye Wamkulu Koposa ndipo ndi tsiku lobwezera chilango kwa adani ake.+ Lupanga lidzadya adaniwo ndi kukhuta ndipo lidzamwa magazi awo kufikira litathetsa ludzu lake. Lidzatero pakuti Yehova wa makamu, Ambuye Wamkulu Koposa,+ ali ndi nsembe imene akufuna kupereka+ m’dziko la kumpoto, m’mphepete mwa mtsinje wa Firate.+

  • Ezekieli 21:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Uuze dziko la Isiraeli kuti, ‘Yehova wanena kuti: “Ine ndidzakulanga.+ Ndidzasolola lupanga langa m’chimake+ ndi kupha anthu ako olungama ndiponso anthu ako oipa.+

  • Zefaniya 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Inunso Aitiyopiya+ mudzaphedwa ndi lupanga langa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena