Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 10:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 M’tsiku limenelo, otsala a Isiraeli+ ndi opulumuka a nyumba ya Yakobo sadzadaliranso yemwe akuwamenya,+ koma ndi mtima wonse adzadalira Yehova, Woyera wa Isiraeli.+

  • Yesaya 66:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Ndidzachita zinthu zazikulu pakati pawo monga chizindikiro.+ Opulumuka ena ndidzawatumiza ku mitundu ya anthu,+ ku Tarisi,+ ku Puli, ndi ku Ludi.+ Ndidzawatumiza kwa anthu odziwa kukoka uta ku Tubala ndi ku Yavani.+ Ndidzawatumiza kuzilumba zakutali,+ kwa anthu amene sanamve mbiri yanga kapena kuona ulemerero wanga.+ Iwo adzanenadi za ulemerero wanga pakati pa mitundu ya anthu.+

  • Yeremiya 44:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Sipadzapezeka aliyense wothawa kapena wopulumuka mwa otsala a Yuda amene alowa m’dziko la Iguputo ndi kukhala mmenemo monga alendo,+ kupatulapo anthu ochepa chabe amene adzathawa. Sipadzapezeka wobwerera kudziko la Yuda kumene akulakalaka kubwerera kuti akakhaleko.’”+

  • Ezekieli 7:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Anthu awo opulumuka adzathawa+ ndipo adzakhala pamapiri ngati njiwa za m’zigwa,+ aliyense akulira chifukwa cha zolakwa zake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena