Yesaya 38:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Ndikungokhalira kulira ngati namzeze* kapena pumbwa.*+Ndikungokhalira kubuula ngati njiwa.+ Maso anga akupenyetsetsa kumwamba motopa. Choncho ndinati:+‘Inu Yehova ine ndapanikizika. Chonde ndithandizeni.’+ Yesaya 59:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Tonsefe tikungolira ngati zimbalangondo ndipo tikungokhalira kubuula momvetsa chisoni ngati njiwa.+ Tinali kuyembekezera chilungamo+ koma sichinabwere. Tinali kuyembekezera chipulumutso koma chakhala nafe kutali.+ Nahumu 2:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Nkhani imeneyi yatsimikiziridwa. Mzindawo udzavulidwa ndi kuchititsidwa manyazi, ndipo anthu ake adzatengedwa.+ Akapolo ake aakazi adzakhala akulira ngati nkhunda+ ndipo adzadziguguda pachifuwa.+
14 Ndikungokhalira kulira ngati namzeze* kapena pumbwa.*+Ndikungokhalira kubuula ngati njiwa.+ Maso anga akupenyetsetsa kumwamba motopa. Choncho ndinati:+‘Inu Yehova ine ndapanikizika. Chonde ndithandizeni.’+
11 Tonsefe tikungolira ngati zimbalangondo ndipo tikungokhalira kubuula momvetsa chisoni ngati njiwa.+ Tinali kuyembekezera chilungamo+ koma sichinabwere. Tinali kuyembekezera chipulumutso koma chakhala nafe kutali.+
7 Nkhani imeneyi yatsimikiziridwa. Mzindawo udzavulidwa ndi kuchititsidwa manyazi, ndipo anthu ake adzatengedwa.+ Akapolo ake aakazi adzakhala akulira ngati nkhunda+ ndipo adzadziguguda pachifuwa.+