Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 74:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndinu amene munang’amba nthaka ndi kupanga akasupe ndi makwawa.+

      Inu munaumitsa mitsinje imene inali kukhala ndi madzi nthawi zonse.+

  • Yesaya 42:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndidzawononga+ mapiri ndi zitunda. Ndidzaumitsa zinthu zonse zimene zinamera mmenemo. Mitsinje ndidzaisandutsa zilumba ndipo madambo ndidzawaumitsa.+

  • Yeremiya 50:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Madzi ake adzawonongedwa ndipo adzauma.+ Dziko limeneli ndi la zifaniziro zogoba,+ ndipo anthu ake amachita zinthu mosaganiza chifukwa cha masomphenya awo ochititsa mantha.

  • Chivumbulutso 16:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mngelo wa 6+ anathira mbale yake pamtsinje waukulu wa Firate,+ ndipo madzi ake anauma,+ kuti njira ya mafumu+ ochokera kotulukira dzuwa ikonzedwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena