Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 50:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 Wamphamvuyo,+ Yehova, Mulungu,+ walankhula+

      Ndipo akuitana dziko lapansi,+

      Kuchokera kotulukira dzuwa mpaka kumene limalowera.+

  • Salimo 118:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Yehova ndiye Mulungu,+

      Ndipo amatipatsa kuwala.+

      Kongoletsani gulu la anthu amene ali pachikondwerero+ ndi nthambi za mitengo,+ anthu inu.

      Likongoletseni mpaka kukafika panyanga za guwa lansembe.+

  • Aroma 1:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Chilengedwere dziko kupita m’tsogolo,+ makhalidwe a Mulungu osaoneka+ ndi maso akuonekera bwino. Makhalidwe a Mulungu amenewa, ngakhalenso mphamvu zake zosatha+ ndiponso Umulungu+ wake, zikuonekera m’zinthu zimene anapanga+ moti anthuwo alibenso chifukwa chomveka chosakhulupirira kuti kuli Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena