Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 7:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma ine ndidzamusiya Farao kuti aumitse mtima wake,+ ndipo ndidzachita zizindikiro ndi zozizwitsa zochuluka m’dziko la Iguputo.+

  • 1 Samueli 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Komanso, mukuumitsiranji mitima yanu mmene Aiguputo ndi Farao anaumitsira mitima yawo?+ Si paja Mulungu atangowakhaulitsa+ analola Aisiraeli kupita, ndipo iwo anapitadi?+

  • Ezekieli 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma a nyumba ya Isiraeli sakafuna kukumvera, chifukwa iwo safuna kundimvera.+ Pakuti anthu onse a nyumba ya Isiraeli ndi amakani ndi osamva.+

  • 2 Akorinto 2:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kwa amene akupita kukawonongedwawo ndife fungo lochokera ku imfa kupita ku imfa,+ koma kwa amene akupita kukapulumukawo ndife fungo lochokera ku moyo kupita ku moyo. Ndipo ndani ali woyenerera kugwira ntchito imeneyi?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena