Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Psompsonani mwanayo+ kuopera kuti Mulungu angakwiye,

      Ndipo mungawonongeke ndi kuchotsedwa panjirayo.+

      Pakuti mkwiyo wake umatha kuyaka mofulumira.+

      Odala ndi onse amene akuthawira kwa iye.+

  • Yesaya 41:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Taona! Onse okupsera mtima adzachita manyazi ndipo adzanyozeka.+ Anthu amene akukangana nawe sadzakhalanso ngati kanthu ndipo adzatha.+

  • Danieli 2:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 “M’masiku a mafumu amenewo,+ Mulungu wakumwamba+ adzakhazikitsa ufumu+ umene sudzawonongedwa ku nthawi zonse.+ Ufumuwo sudzaperekedwa kwa mtundu wina uliwonse wa anthu,+ koma udzaphwanya ndi kuthetsa maufumu ena onsewo,+ ndipo udzakhalapo mpaka kalekale.+

  • Luka 19:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Komanso adani angawa, amene sanafune kuti ine ndikhale mfumu yawo, bwerani nawo kuno muwaphe ine ndikuona.’”+

  • Chivumbulutso 2:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Iyeyo adzakusa anthu ndi ndodo yachitsulo,+ ngati imenenso ine ndailandira kwa Atate wanga. Anthuwo adzaphwanyidwaphwanyidwa ngati mbiya zadothi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena