Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 147:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yehova akumanga Yerusalemu.+

      Anthu okhala mu Isiraeli amene anabalalika akuwasonkhanitsanso pamodzi.+

  • Yesaya 66:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Adzabweretsa abale anu onse kuchokera ku mitundu yonse+ monga mphatso kwa Yehova.+ Adzayenda pamahatchi, pangolo, pangolo zotseka pamwamba, panyulu,* ndi pangamila zazikazi zothamanga,+ popita kuphiri langa loyera,+ ku Yerusalemu. Adzachita zimenezi ngati mmene ana a Isiraeli amabweretsera mphatso m’nyumba ya Yehova, ataiika m’chiwiya choyera,”+ watero Yehova.

  • Obadiya 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Anthu amene anatengedwa kupita kudziko lina kuchokera pachiunda ichi chomenyerapo nkhondo,+ amene ndi ana a Isiraeli, adzatenga zinthu zimene zinali za Akanani+ mpaka kukafika ku Zarefati.+ Anthu amene anatengedwa kuchokera ku Yerusalemu kupita kudziko lina, amene anali ku Sefaradi, adzatenga mizinda ya Negebu kukhala yawo.+

  • Zekariya 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Fulumira Ziyoni!+ Thawa, iwe amene ukukhala ndi mwana wamkazi wa Babulo.+

  • Mateyu 24:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Iye adzatumiza angelo ake ndi kulira kwamphamvu kwa lipenga,+ ndipo adzasonkhanitsa osankhidwa ake+ kuchokera kumphepo zinayi,+ kuchokera kumalekezero a m’mlengalenga mpaka kumalekezero ena.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena