Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 16:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mfumu ya Asuri inamumvera n’kupita ku Damasiko+ ndipo inakalanda mzindawo.+ Anthu a mumzindawo inawatengera ku Kiri,+ ndipo Rezini+ inamupha.

  • Yesaya 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 popeza mwanayo asanadziwe kuitana+ kuti, ‘Ababa!’ kapena ‘Amama!’ anthu adzanyamula chuma cha ku Damasiko ndi katundu wolandidwa ku Samariya n’kupita naye pamaso pa mfumu ya Asuri.”+

  • Zekariya 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Uthenga+ wokhudza dziko la Hadiraki:

      “Awa ndi mawu a Yehova oweruza dziko la Hadiraki, ndipo akuweruzanso Damasiko.+ Pakuti maso a Yehova akuyang’ana anthu+ komanso mafuko onse a Isiraeli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena