Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 8:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Kenako Davide anamanga midzi ya asilikali+ m’dera la Asiriya a ku Damasiko ndipo Asiriyawo anakhala akapolo a Davide moti anali kukhoma msonkho+ kwa iye. Yehova anapitiriza kupulumutsa Davide kulikonse kumene wapita.+

  • 2 Mafumu 14:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Nkhani zina zokhudza Yerobowamu ndi zonse zimene anachita, zochita zake zamphamvu ndiponso mmene anamenyera nkhondo, ndi mmene anabwezeretsera Damasiko+ ndi Hamati+ ku Yuda mu Isiraeli, zinalembedwa m’buku la zochitika za m’masiku a mafumu a Isiraeli.

  • 2 Mbiri 28:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho Yehova Mulungu wake anam’pereka m’manja+ mwa mfumu ya Siriya+ moti Asiriya anam’gonjetsa n’kugwira anthu ake ambiri kupita nawo ku Damasiko.+ Anam’perekanso m’manja mwa mfumu ya Isiraeli+ ndipo inam’gonjetsa n’kupha anthu ake ambirimbiri.

  • Yesaya 7:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Tiyeni tikamenyane ndi dziko la Yuda. Tikalisakaze, tikalilande ndipo tikaligonjetse. Tikaike mfumu ina kuti izilamulira dzikolo. Mfumu yake ikhale mwana wa Tabeeli.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena