Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 22:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Yosiya anachita zoyenera pamaso pa Yehova+ ndipo anayenda m’njira zonse za Davide kholo lake.+ Iye sanapatukire mbali ya kudzanja lamanja kapena lamanzere.+

  • 2 Mafumu 23:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Panalibenso mfumu ina iye asanakhale mfumu imene inabwerera+ kwa Yehova ndi mtima wake wonse, ndi moyo wake wonse,+ ndi mphamvu zake zonse, mogwirizana ndi chilamulo chonse cha Mose. Ngakhale pambuyo pake sipanakhalenso mfumu ina ngati iyeyo.

  • 2 Mbiri 34:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Iye anachita zoyenera pamaso pa Yehova+ ndipo anayenda m’njira za Davide kholo lake.+ Sanapatukire mbali ya kudzanja lamanja kapena lamanzere.+

  • Miyambo 21:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Kuchita zinthu zoyenera ndi zachilungamo kumamusangalatsa kwambiri Yehova, kuposa kupereka nsembe.+

  • Miyambo 31:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsegula pakamwa pako, weruza mwachilungamo ndipo thandiza munthu wosautsika ndi wosauka pa mlandu wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena