Yeremiya 51:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Babulo wakhala kapu yagolide m’dzanja la Yehova+ ndipo waledzeretsa dziko lonse lapansi.+ Mitundu ya anthu yaledzera ndi vinyo wake.+ N’chifukwa chake mitundu ya anthu ikuchita zinthu zamisala.+ Maliro 4:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Kondwa ndipo usangalale,+ iwe mwana wamkazi wa Edomu,+ amene ukukhala m’dziko la Uzi.+Iwenso kapuyo ikupeza.+ Udzaledzera ndipo anthu adzakuona uli maliseche.+ Ezekieli 23:34 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 34 Iwe udzamwa ndi kugugudiza za m’kapuyo,+ ndipo udzatafuna zidutswa za kapuyo ndi kukhadzula mabere ako.+ “Ine ndanena,” watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.’ Nahumu 3:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 “Chotero iwenso udzaledzera,+ ndipo udzabisala.+ Iwenso udzafunafuna malo okhala ndi mpanda wolimba kwambiri kuti utetezeke kwa mdani.+
7 Babulo wakhala kapu yagolide m’dzanja la Yehova+ ndipo waledzeretsa dziko lonse lapansi.+ Mitundu ya anthu yaledzera ndi vinyo wake.+ N’chifukwa chake mitundu ya anthu ikuchita zinthu zamisala.+
21 Kondwa ndipo usangalale,+ iwe mwana wamkazi wa Edomu,+ amene ukukhala m’dziko la Uzi.+Iwenso kapuyo ikupeza.+ Udzaledzera ndipo anthu adzakuona uli maliseche.+
34 Iwe udzamwa ndi kugugudiza za m’kapuyo,+ ndipo udzatafuna zidutswa za kapuyo ndi kukhadzula mabere ako.+ “Ine ndanena,” watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.’
11 “Chotero iwenso udzaledzera,+ ndipo udzabisala.+ Iwenso udzafunafuna malo okhala ndi mpanda wolimba kwambiri kuti utetezeke kwa mdani.+