Yeremiya 38:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 “Yehova wanena kuti, ‘Amene adzapitirize kukhala mumzinda uno adzafa ndi lupanga,+ njala yaikulu+ kapena mliri.+ Koma amene adzadzipereke kwa Akasidi adzakhala ndi moyo. Adzapulumutsa moyo wake, sadzafa ayi.’+ Yeremiya 40:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Gedaliya+ mwana wa Ahikamu+ mwana wa Safani+ analumbira+ pamaso pa akuluakuluwo ndi asilikali awo kuti: “Musaope kutumikira Akasidi. Pitirizani kukhala m’dzikoli n’kumatumikira mfumu ya Babulo ndipo zinthu zikuyenderani bwino.+ Yeremiya 42:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 ‘Ngati mungakhalebe m’dziko lino,+ ndidzakulimbitsani osati kukupasulani, ndidzakubzalani osati kukuzulani,+ pakuti ndidzakumverani chisoni chifukwa cha tsoka limene ndakugwetserani.+
2 “Yehova wanena kuti, ‘Amene adzapitirize kukhala mumzinda uno adzafa ndi lupanga,+ njala yaikulu+ kapena mliri.+ Koma amene adzadzipereke kwa Akasidi adzakhala ndi moyo. Adzapulumutsa moyo wake, sadzafa ayi.’+
9 Gedaliya+ mwana wa Ahikamu+ mwana wa Safani+ analumbira+ pamaso pa akuluakuluwo ndi asilikali awo kuti: “Musaope kutumikira Akasidi. Pitirizani kukhala m’dzikoli n’kumatumikira mfumu ya Babulo ndipo zinthu zikuyenderani bwino.+
10 ‘Ngati mungakhalebe m’dziko lino,+ ndidzakulimbitsani osati kukupasulani, ndidzakubzalani osati kukuzulani,+ pakuti ndidzakumverani chisoni chifukwa cha tsoka limene ndakugwetserani.+