Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 20:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Yehosafati atamva zimenezi anachita mantha+ ndipo anatsimikiza mumtima mwake kuti afunefune Yehova.+ Choncho analengeza kuti Ayuda onse asale kudya.+

  • Nehemiya 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pa tsiku la 24 la mwezi umenewu+ ana a Isiraeli anasonkhana pamodzi. Iwo anali kusala kudya+ atavala ziguduli*+ ndiponso atadzithira dothi+ kumutu.

  • Esitere 4:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Pitani mukasonkhanitse Ayuda onse amene angapezeke ku Susani+ ndipo musale kudya+ m’malo mwa ine. Musadye kapena kumwa kwa masiku atatu,+ usana ndi usiku. Inenso pamodzi ndi atsikana anga onditumikira+ tisala kudya. Pamenepo, ngakhale kuti ndi zosemphana ndi lamulo, ndidzapita kwa mfumu, ndipo ngati n’kufa,+ ndife.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena