Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 24:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Iye ataona Akeni,+ anapitirizanso mawu ake a ndakatulo, kuti:

      “Mokhala mwanu ndi mokhazikika, malo okhala inu ali pathanthwe.

  • Salimo 55:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ndipo ndikunena kuti: “Ndikanakhala ndi mapiko ngati njiwa!+

      Ndikanauluka ndi kukakhala kwina.+

  • Nyimbo ya Solomo 2:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iwe njiwa yanga,+ tuluka m’malo obisika a pathanthwe. Tuluka pamalo osaoneka m’mphepete mwa njira yotsetsereka. Ndikufuna ndione thupi lako lokongola.+ Ndikufuna kumva mawu ako, chifukwa mawu ako ndi okoma ndipo iweyo ndiwe wokongola.’”+

  • Yeremiya 49:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Iwe unachititsa anthu kunjenjemera ndiponso unali ndi mtima wodzikuza,+ koma zimenezi zakunyenga, iwe amene ukukhala m’malo obisika a m’thanthwe pamwamba pa phiri. Ngakhale kuti umamanga chisa chako pamwamba kwambiri ngati chiwombankhanga+ ndidzakugwetsa kuchoka pamenepo,”+ watero Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena