Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 94:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Nyamukani inu Woweruza dziko lapansi.+

      Perekani chilango kwa anthu odzikweza.+

  • Miyambo 8:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kuopa Yehova kumatanthauza kudana ndi zoipa.+ Ndimadana ndi kudzikweza, kunyada,+ njira yoipa ndiponso pakamwa ponena zopotoka.+

  • Yesaya 16:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ife tamva za kunyada kwa Mowabu, kuti ndi wonyada kwambiri.+ Tamva za kudzikweza kwake, kunyada kwake, ndi mkwiyo wake.+ Zolankhula zake zodzitukumula sizidzachitika.+

  • Zefaniya 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Anthu amenewo adzaona zimenezi chifukwa cha kunyada kwawo,+ komanso chifukwa chakuti anali kunyoza ndi kudzikweza pamaso pa anthu a Yehova wa makamu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena