Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 55:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Inu Yehova, sokonezani anthu oipa, ndipo sokonezani zonena zawo,+

      Pakuti ndaona ziwawa ndi mikangano mumzinda.+

  • Yeremiya 20:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Nthawi zonse ndikalankhula mawu anu ndimalira. Ndimanena za chiwawa ndi kufunkhidwa,+ pakuti mawu a Yehova achititsa kuti ndizinyozedwa ndi kutonzedwa tsiku lonse.+

  • Ezekieli 7:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chiwawa chasanduka ndodo ya zoipa.+ Anthuwo paokha, chuma chawo, ndiponso kutchuka kwawo, sizidzawapulumutsa ku chilango.

  • Mika 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Iwo alakalaka minda ya anthu ena ndipo ailanda.+ Alakalakanso nyumba za anthu ena n’kuzitenga kukhala zawo.+ Atenga mwachinyengo cholowa cha munthu ndi cha banja lake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena