Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 “Usalakelake nyumba ya mnzako. Usalakelake mkazi wa mnzako,+ kapolo wake wamwamuna, kapolo wake wamkazi, ng’ombe yake, bulu wake, kapena chilichonse cha mnzako.”+

  • 1 Mafumu 21:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ahabu anauza Naboti kuti: “Ndipatse+ munda wako wa mpesawu+ kuti ukhale munda+ wanga woti ndizilimamo masamba,+ chifukwa uli pafupi ndi nyumba yanga. M’malo mwa munda wakowu ndikupatsa munda wina wa mpesa, wabwino kuposa umenewu. Ngati ungafune,+ ndiugula ndi ndalama.”

  • Nehemiya 5:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chonde, lero abwezereni minda yawo ya tirigu,+ minda yawo ya mpesa, minda yawo ya maolivi, nyumba zawo ndi limodzi mwa magawo 100 a ndalama, tirigu, vinyo watsopano ndi mafuta zimene munalandira kwa iwo monga chiwongoladzanja.”

  • Yesaya 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tsoka kwa anthu amene akuwonjezera nyumba zina panyumba zawo,+ ndiponso amene akuwonjezera minda ina kuminda yawo, mpaka malo onse kutha,+ ndipo amuna inu mwayamba kukhala nokhanokha m’dzikoli.

  • Ezekieli 22:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Anthu a m’dzikolo abera anthu pochita zachinyengo+ ndiponso zauchifwamba.+ Iwo akuzunza anthu osautsika ndi osauka.+ Abera mlendo pochita zachinyengo komanso zopanda chilungamo.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena