1 Samueli 7:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Ndiyeno zimene zinachitika n’zakuti, kuchokera pamene Likasa linayamba kukhala ku Kiriyati-yearimu, panapita nthawi yaitali mpaka zinakwana zaka 20. Izi zili choncho, nyumba yonse ya Isiraeli inayamba kulirira Yehova.+ Yesaya 29:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Ariyeli ndidzamukhwimitsira zinthu,+ ndipo padzakhala kulira ndi kumva chisoni.+ Kwa ine, iye adzakhala ngati malo osonkhapo moto paguwa lansembe la Mulungu.+ Mika 2:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Pa tsikulo munthu adzanena mwambi+ wokhudza anthu inu ndipo ndithu adzakuimbirani nyimbo ya maliro.+ Anthu adzanena kuti: “Ife talandidwa zinthu zathu!+ Cholowa cha anthu amtundu wathu chaperekedwa kwa anthu ena.+ Talandidwa cholowa chathu. Iye wapereka minda yathu kwa anthu osakhulupirika.”
2 Ndiyeno zimene zinachitika n’zakuti, kuchokera pamene Likasa linayamba kukhala ku Kiriyati-yearimu, panapita nthawi yaitali mpaka zinakwana zaka 20. Izi zili choncho, nyumba yonse ya Isiraeli inayamba kulirira Yehova.+
2 Ariyeli ndidzamukhwimitsira zinthu,+ ndipo padzakhala kulira ndi kumva chisoni.+ Kwa ine, iye adzakhala ngati malo osonkhapo moto paguwa lansembe la Mulungu.+
4 Pa tsikulo munthu adzanena mwambi+ wokhudza anthu inu ndipo ndithu adzakuimbirani nyimbo ya maliro.+ Anthu adzanena kuti: “Ife talandidwa zinthu zathu!+ Cholowa cha anthu amtundu wathu chaperekedwa kwa anthu ena.+ Talandidwa cholowa chathu. Iye wapereka minda yathu kwa anthu osakhulupirika.”