Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Anam’peza m’dziko lachipululu,+

      M’chipululu chopanda kanthu, molira zilombo zakutchire.+

      Pamenepo anayamba kum’zungulira,+ kum’samalira,+

      Kum’teteza monga mwana wa diso lake.+

  • Salimo 77:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mwatsogolera anthu anu ngati nkhosa,+

      Kudzera mwa Mose ndi Aroni.+

  • Salimo 78:54
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 54 Kenako anawalowetsa m’dziko lake lopatulika,+

      M’dera lamapiri ili limene dzanja lake lamanja linatenga.+

  • Salimo 136:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yamikani amene anayendetsa anthu ake m’chipululu:+

      Pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+

  • Yesaya 63:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 amene anawawolotsa pamadzi amphamvu moti sanapunthwe, mofanana ndi hatchi m’chipululu?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena