7 ine ndakutambasulirani dzanja langa,+ ndipo ndidzakuperekani kwa mitundu ina ya anthu monga zofunkha. Ndidzakuphani ndi kukuchotsani pakati pa mitundu ina ya anthu ndi kukuwonongani kuti musapezekenso m’dziko.+ Ndidzakufafanizani,+ ndipo mudzadziwa kuti ine ndine Yehova.’