Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 24:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Uuse moyo mosatulutsa mawu. Anthu akufa usawalire maliro.+ Uvale chovala chakumutu+ ndipo uvale nsapato zako.+ Usaphimbe ndevu zako zapamlomo,+ ndipo usadye chakudya chimene anthu angakupatse.”+

  • Hoseya 9:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Iye sadzapitiriza kupatsa Yehova nsembe zavinyo.+ Mulungu sadzakondwera ndi nsembe zake,+ chifukwa zili ngati chakudya cha pamaliro.+ Onse amene adzadya chakudyacho adzadziipitsa. Chakudya chawo chidzakhala chongokhutitsa iwowo basi, ndipo sichidzalowa m’nyumba ya Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena