Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 137:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Kumeneko, amene anatigwira ukapolo anatiuza kuti tiwaimbire nyimbo,+

      Ndipo otinyozawo anatipempha kuti tiwasangalatse.+ Iwo anati:

      “Tiimbireni imodzi mwa nyimbo za ku Ziyoni.”+

  • Miyambo 24:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mdani wako akagwa usamasangalale ndipo akapunthwa, mtima wako usamakondwere,+

  • Maliro 2:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Adani ako onse akukutsegulira pakamwa.+

      Akuimba mluzu ndi kukukukutira mano.+ Iwo akunena kuti: “Ameneyu timumeza.+

      Ndithu, lero ndi tsiku limene takhala tikuyembekezera.+ Lafikadi! Taliona!”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena