Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 22:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 N’chifukwa chake ndanena kuti: “Musandiyang’anitsitse. Ine ndikulira mopwetekedwa mtima+ ndipo anthu inu musaumirire kunditonthoza pamene ndikulirira mwana wamkazi wa anthu anga, yemwe walandidwa katundu.+

  • Yeremiya 4:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 M’mimba mwanga ine, m’mimba mwanga! Ndikumva kupweteka kwambiri mumtima mwanga.+ Mtima wanga ukuvutika.+ Sindingathe kukhala chete pakuti ndamva kulira kwa lipenga la nyanga ya nkhosa, chizindikiro chochenjeza cha nkhondo.+

  • Ezekieli 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pamene amunawo anali kupha anthu, ine ndinatsala ndekha wamoyo, ndipo ndinagwada n’kuwerama mpaka nkhope yanga pansi.+ Kenako ndinafuula kuti: “Kalanga ine,+ Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa! Kodi muwononga otsala onse a Isiraeli pamene mukukhuthulira ukali wanu pa Yerusalemu?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena