Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 17:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Wonyoza munthu wosauka amanyoza amene anam’panga.+ Amene amasangalala ndi tsoka la wina sadzalephera kulangidwa.+

  • Miyambo 24:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mdani wako akagwa usamasangalale ndipo akapunthwa, mtima wako usamakondwere,+

  • Ezekieli 26:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Iwe mwana wa munthu, Turo+ wanena Yerusalemu+ kuti, ‘Eyaa! Zakhala bwino! Mzindawo wathyoledwa.+ Mzinda umene unali kukopa anthu a mitundu ina+ wathyoledwa. Tsopano ine zinthu zindiyendera bwino. Ndilemera chifukwa mzindawo wawonongedwa.’+

  • Ezekieli 35:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Iwe mwana wa munthu, yang’ana+ kudera lamapiri la Seiri+ ndipo ulosere zoipa zimene zidzachitikire deralo.+

  • Ezekieli 35:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iwe udzadziwa kuti ine Yehova, ndinamva mawu onse achipongwe amene unanenera mapiri a ku Isiraeli.+ Pakuti iwe unanena kuti: “Mapiri aja awonongedwa. Aperekedwa kwa ife kuti akhale chakudya chathu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena