Genesis 9:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Koma musadye+ nyama pamodzi ndi magazi+ ake, amene ndiwo moyo+ wake. Levitiko 17:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 N’chifukwa chake ndauza ana a Isiraeli kuti: “Pasapezeke munthu wodya magazi ndipo pasapezeke mlendo wokhala pakati panu+ wodya magazi.”+ Deuteronomo 12:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Koma musadye magazi ake.+ Muziwathira panthaka ngati madzi.+ 1 Samueli 14:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Zitatero, anthuwo anayamba kuthamangira zofunkha mosusuka+ ndi kutenga nkhosa, ng’ombe ndi ana a ng’ombe. Zimenezi anali kuziphera pansi, ndipo anthuwo anayamba kudya nyamayo pamodzi ndi magazi ake.+ Machitidwe 15:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 kupitiriza kupewa zinthu zoperekedwa nsembe kwa mafano,+ magazi,+ zopotola,+ ndi dama.+ Mukamapewa zinthu zimenezi mosamala kwambiri,+ zinthu zidzakuyenderani bwino. Tikukufunirani zabwino zonse!”
12 N’chifukwa chake ndauza ana a Isiraeli kuti: “Pasapezeke munthu wodya magazi ndipo pasapezeke mlendo wokhala pakati panu+ wodya magazi.”+
32 Zitatero, anthuwo anayamba kuthamangira zofunkha mosusuka+ ndi kutenga nkhosa, ng’ombe ndi ana a ng’ombe. Zimenezi anali kuziphera pansi, ndipo anthuwo anayamba kudya nyamayo pamodzi ndi magazi ake.+
29 kupitiriza kupewa zinthu zoperekedwa nsembe kwa mafano,+ magazi,+ zopotola,+ ndi dama.+ Mukamapewa zinthu zimenezi mosamala kwambiri,+ zinthu zidzakuyenderani bwino. Tikukufunirani zabwino zonse!”