Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 39:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Chimafunafuna chakudya kuchokera pamenepo.+

      Maso ake amaona kutali kwambiri.

  • Miyambo 30:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Njira ya chiwombankhanga m’mlengalenga, njira ya njoka pamwala, njira ya ngalawa pakatikati pa nyanja,+ ndiponso njira ya mwamuna ndi mtsikana.+

  • Ezekieli 10:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kerubi aliyense anali ndi nkhope zinayi.+ Nkhope yoyamba inali ya kerubi. Nkhope yachiwiri inali ya munthu.+ Nkhope yachitatu inali ya mkango, ndipo nkhope yachinayi inali ya chiwombankhanga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena