Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 25:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Iye anatentha nyumba ya Yehova,+ nyumba ya mfumu,+ nyumba zonse za mu Yerusalemu,+ ndi nyumba ya munthu aliyense wotchuka.+

  • Salimo 120:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Adzakupatsa mivi yakuthwa ya munthu wamphamvu,+

      Pamodzi ndi makala amoto a mtengo wa m’chipululu.+

  • Salimo 140:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Muwakhuthulire makala oyaka moto pamutu pawo.+

      Muwachititse kugwera m’moto+ ndi m’madzi akuya kuti asanyamukenso.+

  • Chivumbulutso 8:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Koma nthawi yomweyo, mngeloyo anatenga chiwiya chofukiziramo chija, n’kudzazamo moto+ umene anapala paguwa lansembe, ndi kuuponyera kudziko lapansi.+ Ndiyeno kunagunda mabingu,+ kunamveka mawu, ndipo kunachita mphezi+ ndi chivomezi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena